Mawu a M'munsi
a Isaki, yemwe anali mwana wa Abulahamu anavutikanso ndi chisoni kwa nthawi yaitali mayi ake atamwalira. Monga tafotokozera m’nkhani yakuti, “Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo” yomwe ili m’magaziniyi, iye ankamvabe chisoni ngakhale kuti panali patatha zaka zitatu.—Genesis 24:67.