Mawu a M'munsi
a Zimenezi zinachitika chakumadzulo. Ndipo nkhaniyi sisonyeza kuti Rabeka anakhalitsa kwambiri kuchitsimeko kapenanso kuti anakafika kwawo anthu atagona. Sisonyezanso kuti winawake anamulondola kuchitsimeko ataona kuti akuchedwa kubwera.