Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Lemba la Ezekieli 37:1-14 komanso la Chivumbulutso 11:7-12, limanena za kumasulidwa kwa anthu a Mulungu mu ukapolo komwe kunachitika mu 1919. Komabe ulosi wa pa Ezekieliwu ukunena za kumasulidwa kwa anthu onse a Mulungu amene anakhala mu ukapolo kwa nthawi yaitali. Pamene ulosi wa pa Chivumbulutso ukunena za kuyambiranso kwa kagulu ka abale odzozedwa komwe kanasankhidwa mu 1919 ndipo kakhala kakutsogolera anthu a Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena