Mawu a M'munsi
a Mwachitsanzo, chikalata cholengeza kuti dziko la United States ndi lodziimira palokha (U.S. Declaration of Independence), chinalembedwa pachikopa. Panopa padutsa zaka zosapitirira 250 kuchokera nthawi yomwe chikalatachi chinalembedwa, koma zilembo zake zimavuta kuwerenga chifukwa zinafufutika.