Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pamene Yesu ankanena za chizindikiro cha masiku otsiriza anatchula mafanizo angapo. N’zochititsa chidwi kuti poyamba anatchula za “kapolo wokhulupirika ndi wanzeru” yemwe ndi kagulu ka abale odzozedwa amene akutsogolera anthu a Mulungu. (Mat. 24:45-47) Kenako anafotokoza mafanizo onena za Akhristu odzozedwa onse. (Mat. 25:1-30) Pomaliza ananena za Akhristu odzakhala padziko lapansi amene akuthandiza abale a Khristu. (Mat. 25:31-46) Mofanana ndi zimenezi, m’masiku athu ano, ulosi wa Ezekieli unayamba kukwaniritsidwa pa anthu amene ali ndi chiyembekezo chodzapita kumwamba. Ngakhale kuti ufumu wa mafuko 10 sukuimira anthu odzakhala padziko lapansi, mgwirizano umene wafotokozedwa mu ulosiwu, umatikumbutsa mgwirizano umene uli pakati pa Akhristu odzakhala padziko lapansi ndi odzapita kumwamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena