Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Zikuoneka kuti panali akatswiri ena m’mbuyomo amene anamasulirapo Baibulo la Chipangano Chatsopano m’Chiheberi. Mmodzi wa anthu amenewa anali Simon Atoumanos ndipo analimasulira cha m’ma 1360. Wina anali Oswald Schreckenfuchs, wa ku Germany ndipo anamasulira Baibulo lake cha m’ma 1565. Mabaibulo amenewa sanasindikizidwe ndipo sapezeka masiku ano.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena