Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b N’zodziwikiratu kuti anthu ena amene adzapulumuke nkhondo ya Aramagedo adzakhala olumala. Yesu ali padzikoli, anachiritsa anthu okhala ndi “zofooka zilizonse” ndipo zimenezi zikusonyeza zimene iye adzachitire anthu opulumuka pa Aramagedo, osati oukitsidwa. (Mat. 9:35) N’zosakayikitsa kuti anthu amene anamwalira adzaukitsidwa ndi matupi abwinobwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena