Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Koma chimene anthuwa sadziwa n’chakuti ngakhale munthu amene amayendera maganizo akeake amakhala akutsatira winawake. Kaya munthu akuganizira nkhani zikuluzikulu monga mmene moyo unayambira kapena zing’onozing’ono monga kavalidwe, sangapeweretu kuyendera maganizo a anthu ena. Koma aliyense akhoza kusankha kuti aziyendera maganizo a ndani.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena