Mawu a M'munsi
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Ophunzira a Khristu samangophunzira zimene Yesu ankaphunzitsa koma amatsatiranso mfundozo pa moyo wawo. Amayesetsa kutsatira mapazi a Yesu mosamala kwambiri, kapena kuti kutengera chitsanzo chake.—1 Pet. 2:21.