Mawu a M'munsi
c MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Munthu amene akupita kutchuthi watenga kapepala kwa a Mboni kubwalo la ndege. Tsiku lina akukaona malo, waona a Mboni ena akulalikira m’malo opezeka anthu ambiri. Atabwera kutchuthi, a Mboni afika kunyumba kwawo.