Mawu a M'munsi
a M’Baibulo, kutchova juga kumatchulidwa mwachindunji kamodzi kokha pa nkhani yonena za asilikali a Roma omwe anachita maere, kapena kuti “anatchova juga” pa chovala cha Yesu.—Mateyu 27:35; Yohane 19:23, 24; Contemporary English Version; Good News Translation.