Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yehova ndi Atate wachikondi, wanzeru komanso woleza mtima. Makhalidwewa amaonekera bwino tikaganizira mmene analengera zinthu zonse komanso cholinga chake chodzaukitsa anthu amene anamwalira. Munkhaniyi, tikambirana mafunso ena omwe tingakhale nawo okhudza kuukitsidwa kwa akufa ndipo tiona mmene tingasonyezere kuyamikira Yehova chifukwa cha chikondi, nzeru komanso kuleza mtima kwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena