Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kodi mumakhala m’dziko lomwe mumatha kulambira Yehova mwaufulu? Ngati ndi choncho, kodi mukuigwiritsa ntchito bwanji nthawi ya mtendereyi? Nkhaniyi ikuthandizani kuona zomwe mungachite kuti muzitsanzira Asa yemwe anali Mfumu ya Yuda komanso Akhristu a munthawi ya atumwi. Anthu amenewa anachita zinthu mwanzeru pa nthawi imene zinthu zinali bwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena