Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Tsiku la 27 March 2021, lidzakhala lapadera kwambiri kwa Mboni za Yehova. Madzulo a tsiku limeneli tidzachita mwambo wokumbukira imfa ya Khristu. Anthu ambiri amene adzapezeke pamwambowu ndi amene Yesu anawatchula kuti a “nkhosa zina.” Kodi mu 1935, a Mboni za Yehova anadziwa mfundo yachoonadi iti? Kodi a nkhosa zina akuyembekezera kudzasangalala ndi zinthu ziti pambuyo pa chisautso chachikulu? Nanga amatamanda bwanji Mulungu ndi Khristu akapezeka pamwambo wa Chikumbutso?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena