Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mtumwi Yohane ayenera kuti ndi “wophunzira amene Yesu anali kumukonda kwambiri.” (Yoh. 21:7) Choncho ngakhale kuti iye anali wachinyamata, ayenera kuti anali ndi makhalidwe ambiri abwino. Patapita nthawi, ali wachikulire, Yehova anamugwiritsa ntchito kulemba zambiri zokhudza chikondi. Munkhaniyi, tikambirana zina zimene iye analemba komanso zomwe tingaphunzire pa chitsanzo chake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena