Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti Yesu anali Mphunzitsi wamkulu kuposa onse amene anakhalako, anthu ambiri m’nthawi yake anamukana. N’chifukwa chiyani? Munkhaniyi, tikambirana zifukwa 4. Tikambirananso chifukwa chake anthu ambiri masiku ano sakhulupirira zimene otsatira enieni a Yesu amanena komanso kuchita. Ndipo tiphunziranso chifukwa chake tiyenera kukhulupirira kwambiri Yesu kuti tisakhumudwe n’kusiya kumutsatira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena