Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Popeza si ife angwiro, nthawi zina tingalankhule kapena kuchita zinthu zimene zingakhumudwitse abale ndi alongo athu. Ndiye zikatere tiyenera kuchita chiyani? Kodi timayesetsa kuti tikhalenso pamtendere ndi abale athuwo? Nanga kodi timapepesa mofulumira? Kapena kodi timaona kuti ngati akhumudwa ndi vuto lawo osati lathu? Kapenanso bwanji ngati sitichedwa kukhumudwa ndi zimene alankhula kapena kuchita? Kodi timadzikhululukira n’kumanena kuti ndi mmene ndilili basi? Kapena kodi timaona kuti limeneli ndi vuto lathu ndipo tiyenera kusintha?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena