Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yehova watipatsa mwayi, osati wogwira ntchito yolalikira yokha, koma kutinso tiziphunzitsa anthu kusunga zinthu zonse zimene Yesu analamula. Ndiye n’chiyani chimatilimbikitsa kuti tiziphunzitsa ena? Kodi ndi mavuto otani amene timakumana nawo tikamalikira komanso kuphunzitsa anthu kuti akhale otsatira a Yesu? Nanga tingatani kuti mavutowo asatilepheretse kugwira ntchitoyi? Munkhaniyi, tikambirana mayankho a mafunso amenewa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena