Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: Mlongo wakhala akupemphera kwa Yehova nthawi zonse kuyambira ali wamng’ono. Ali mwana makolo ake anamuphunzitsa kupemphera. Ali mtsikana anayamba upainiya ndipo nthawi ndi nthawi ankapempha Yehova kuti adalitse utumiki wake. Patapita zaka mwamuna wake atayamba kudwala kwambiri, iye ankapempha Yehova kuti amuthandize kupirira mayesero amenewo. Panopa ndi wamasiye ndipo amapemphera nthawi zonse n’kumakhulupirira kuti Atate wake wakumwamba ayankha mapemphero ake monga mmene wakhala akuchitira m’mbuyo monsemu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena