Mawu a M'munsi
a Yesu anatilimbikitsa kuti tilowe pachipata chopapatiza chomwe msewu wake ukulowera kumoyo. Anatilangizanso kuti tizikhala pamtendere ndi Akhristu anzathu. Kodi ndi mavuto otani amene tingakumane nawo tikamatsatira malangizo akewa? Nanga tingatani kuti tilimbane nawo?