Mawu a M'munsi
d MAWU OFOTOKOZERA ZITHUNZI: Tikamayendabe pamsewu “wopanikiza” womwe uli ndi zotchingira zotiteteza zomwe Yehova Mulungu watipatsa, timapewa zinthu zoopsa monga kuonera zolaula, kuchita zachiwerewere komanso sitingagonje tikamakakamizidwa kuti tiike maphunziro apamwamba pamalo oyamba pa moyo wathu.