Mawu a M'munsi
a Yakobo anakulira m’banja limenenso Yesu anakulira. Iye ankamudziwa bwino kwambiri Mwana wangwiro wa Mulungu kuposa anthu ambiri pa nthawiyo. Yakobo anadzakhala mmodzi mwa abale amene ankatsogolera mpingo mu nthawi ya atumwi. Munkhaniyi tiona zimene tingaphunzire pa moyo wa mn’gono wake wa Yesu komanso zimene anaphunzitsa.