Mawu a M'munsi
b Munkhaniyi Yakobo tizimutchula kuti mchimwene wake wa Yesu. Kwenikweni iye anali m’bale wake wa Yesu chifukwa onsewa anabadwa kwa mayi mmodzi. Ndipo zikuoneka kuti iye ndi amene analemba buku la m’Baibulo lomwe limadziwika ndi dzina lake.