Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Timoteyo anali mlaliki waluso wa uthenga wabwino. Komabe Paulo anamulimbikitsa kuti apitirizebe kupita patsogolo mwauzimu. Kumvera malangizowa, kukanachititsa kuti Yehova azimugwiritsa ntchito ndiponso azithandiza kwambiri abale ndi alongo ake. Kodi inunso mofanana ndi Timoteyo mukufunitsitsa kuti muzichita zambiri potumikira Yehova komanso Akhristu anzanu? Mosakayikira. Ndiye kodi ndi zolinga ziti zimene zingakuthandizeni? Nanga mungatani kuti mukhale nazo n’kumazikwaniritsa?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena