Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Si nthawi zonse pamene mantha angakhale oipa. Mantha ena angatiteteze pomwe ena angachititse kuti tikumane ndi mavuto. Satana angagwiritse ntchito mantha potichititsa kusankha zolakwika. N’zoonekeratu kuti timafunika kuyesetsa kuti tisamakhale ndi mantha amenewo. Kodi n’chiyani chingatithandize? Monga mmene tionere munkhaniyi, tikamakhulupirira kuti Yehova ali kumbali yathu komanso amatikonda, sitingamaope chilichonse.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena