Mawu a M'munsi
d MAWU OFOTOKOZERA CHITHUNZI: Mkulu akuyendera m’bale wina yemwe chikhulupiriro chake chafooka. Iye akumusonyeza zithunzi za Sukulu ya Utumiki Waupainiya yomwe analowera limodzi zaka zambiri m’mbuyomo. Zithunzizo zikumukumbutsa mmene ankasangalalira pa nthawiyo. M’baleyo akufuna kuyambiranso kusangalala ngati mmene ankachitira pamene ankatumikira Yehova. Patapita nthawi, iye anayambiranso kusonkhana.