Mawu a M'munsi
a Baibulo limalimbikitsa Akhristu kuti azimvera olamulira akuluakulu omwe ndi maboma a m’dzikoli. Koma maboma ena amachita kuonetseratu kuti amatsutsa Yehova ndi atumiki ake. Ndiye kodi tingatani kuti tizimvera olamulirawa koma n’kumakhalabe okhulupirika kwa Yehova?