Mawu a M'munsi
a Munkhaniyi tikambirana zinthu zitatu zomwe zinathandiza mneneri Ezekieli kuti akwanitse kugwira ntchito yolalikira imene anapatsidwa. Kuona mmene Yehova anathandizira mneneri wakeyu kutithandiza kuti tizikhulupirira kwambiri kuti Yehova angatithandizenso ifeyo kuti tizikwaniritsa utumiki wathu.