Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mtumwi Paulo analangiza Akhristu anzake kuti asamaganize kapena kuchita zinthu potengera nzeru za nthawi ino. Malangizo amenewatu ndi othandizanso kwa ife masiku ano. Sitiyenera kulola kuti zochitika za m’dzikoli zizikhudza kaganizidwe ndi zochita zathu ngakhale pang’ono. Kuti izi zitheke, tiyenera kupitiriza kusintha kaganizidwe kathu ngati tazindikira kuti sikakugwirizana ndi zimene Mulungu amafuna. Munkhaniyi, tikambirana mmene tingachitire zimenezi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena