Mawu a M'munsi
b Katswiri wina wa Baibulo anafotokoza kuti: “Kumadera a kum’mawa kuchereza alendo kunali kofunika kwambiri ndipo wocherezayo ankafunika kuonetsetsa kuti alendowo apatsidwa zambiri kuposa zimene akufunikira. Ndipo makamaka paphwando laukwati, eni ukwatiwo ankafunika kupatsa alendo awo zakudya komanso zakumwa zambiri.”