Mawu a M'munsi
a Gidiyoni anasankhidwa ndi Yehova kuti azitsogolera komanso kuteteza anthu a Mulungu pa nthawi yovuta kwambiri mumbiri ya Aisiraeli. Iye anachita utumikiwu mokhulupirika kwa zaka pafupifupi 40. Komabe iye anakumana ndi mavuto ambiri. Tikambirana mmene chitsanzo chake chingathandizire akulu masiku ano akamakumana ndi mavuto.