Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kudziwa malire athu n’kogwirizana ndi kudzichepetsa. Timasonyeza kuti tikuzindikira malire athu podziona moyenera n’kumadziwa kuti pali zina zomwe sitingakwanitse. Timasonyeza kuti ndife odzichepetsa tikamalemekeza ena komanso kuwaona kukhala otiposa. (Afil. 2:3) Kawirikawiri, munthu amene amazindikira zomwe sangakwanitse amakhalanso wodzichepetsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena