Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Achinyamata, Yehova amadziwa kuti mumakumana ndi mavuto amene angachititse kuti musakhale naye pa ubwenzi. Kodi mungatani kuti muzisankha mwanzeru zinthu zomwe zingasangalatse Atate wanu wakumwamba? Munkhaniyi tikambirana zitsanzo za anyamata atatu amene anadzakhala mafumu a Yuda. Tiyeni tione zimene mungaphunzire pa zimene iwo anasankha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena