Mawu a M'munsi
a Popeza si ife angwiro, nthawi zina timavutika kukhala omvera ngakhale pamene munthu amene akutipatsa malangizoyo ali ndi udindo woyenera kuchita zimenezo. Munkhaniyi, tiona mmene timapindulira ngati timamvera makolo athu, “olamulira akuluakulu” ndiponso abale amene amatsogolera mumpingo.