Mawu a M'munsi
b Kuti mudziwe zimene mungachite polankhulana ndi makolo anu zokhudza malamulo omwe mukuona kuti ndi ovuta kuwamvera, onani nkhani ya pa jw.org yamutu wakuti, “Kodi Ndingakambirane Bwanji ndi Makolo Anga za Malamulo Amene Anakhazikitsa?”