Mawu a M'munsi
a Kuphunzira Baibulo kungatithandize kuti tikhale osangalala kwa moyo wathu wonse ndipo kungatithandize kuti tikhale pa ubwenzi wolimba ndi Atate wathu wakumwamba. Munkhaniyi tiona zimene tingachite kuti tizimvetsa bwino m’lifupi, m’litali, kukwera ndi kuzama kwa Mawu a Mulungu.