Mawu a M'munsi
a Mfundo imodzi yozama yopezeka m’Mawu a Mulungu ndi yokhudza kachisi wamkulu wauzimu. Kodi kachisi ameneyu ndi chiyani? Munkhaniyi tikambirana mfundo zopezeka m’buku la Aheberi zokhudza kachisiyu. Tikukhulupirira kuti kuphunzira nkhaniyi kukuthandizani kuti muziyamikira kwambiri mwayi wanu wolambira Yehova.