Mawu a M'munsi
c Chakumapeto kwa zaka 40 zimene anayenda m’chipululu, Aisiraeli anatenga ziweto zambiri za mitundu imene anaigonjetsa pankhondo. (Num. 31:32-34) Ngakhale zinali choncho, iwo anapitiriza kudya mana mpaka pamene anakalowa m’Dziko Lolonjezedwa.—Yos. 5:10-12.