Mawu a M'munsi
a Alongo athu achitsikananu, dziwani kuti timakukondani ndipo ndinu amtengo wapatali kwambiri mumpingo. Mukhoza kukula mwauzimu mukamayesetsa kuti mukhale ndi makhalidwe abwino, mukamaphunzira maluso othandiza komanso mukamakonzekera maudindo anu am’tsogolo. Mukatero mudzapeza madalitso ambiri potumikira Yehova.