Mawu a M'munsi
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Mkhristu wolimba mwauzimu amatsogoleredwa ndi mzimu wa Mulungu osati nzeru za anthu. Iye amatengera chitsanzo cha Yesu, amayesetsa kuti akhale pa ubwenzi wolimba ndi Yehova ndiponso amasonyeza chikondi chenicheni kwa anthu ena.