Mawu a M'munsi
e Onani zithunzi komanso bokosi lakuti “Kodi Abale ndi Alongo Anachita Zotani?” M’bale yemwe anasiya kusonkhana akuchita manyazi kuti akalowe mu Nyumba ya Ufumu, koma kenako akulimba mtima n’kukalowa. Akulandiridwa bwino ndipo akucheza ndi Akhristu anzake.