Mawu a M'munsi
b Mawu a Mulungu salimbikitsa kupatukana ndipo amafotokoza momveka bwino kuti anthu akapatukana sakhala ndi ufulu wokwatira kapena kukwatiwanso. Koma pali mavuto ena akuluakulu omwe angachititse Akhristu kupatukana. Onani mawu a kumapeto 4, “Kodi Okwatirana Angapatukane pa Zifukwa Ziti?” mu buku la Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale.