Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Kusonkhanitsa “zinthu zakumwamba” komwe Paulo anatchula pa Aefeso 1:10, n’kosiyana ndi kusonkhanitsa “osankhidwa” ake komwe Yesu anatchula pa Mateyu 24:31 ndi Maliko 13:27. Paulo ankanena za nthawi imene Yehova amasankha anthu oti akalamulire limodzi ndi Yesu powadzoza ndi mzimu wake woyera. Pomwe Yesu ankanena za nthawi imene odzozedwa omwe adzakhale adakali padzikoli adzasonkhanitsidwe kupita kumwamba pa nthawi ya chisautso chachikulu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena