Mawu a M'munsi
a TANTHAUZO LA MAWU ENA: M’Baibulo, mawu akuti “tchimo” amanena za makhalidwe monga kuba, chiwerewere kapena kupha. (Eks. 20:13-15; 1 Akor. 6:18) M’malemba ena, mawu akuti “tchimo” anganene za uchimo umene tinatengera pobadwa ngakhale kuti timakhala tisanachite choipa chilichonse.