Mawu a M'munsi
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Chimwemwe ndi khalidwe limene timakhala nalo mothandizidwa ndi mzimu wa Mulungu. (Agal. 5:22) Kuti munthu akhaledi wosangalala amafunika kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova.
b TANTHAUZO LA MAWU ENA: Chimwemwe ndi khalidwe limene timakhala nalo mothandizidwa ndi mzimu wa Mulungu. (Agal. 5:22) Kuti munthu akhaledi wosangalala amafunika kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova.