Mawu a M'munsi
a Kuti mudziwe zambiri za mmene udindo wa Yesu monga Mkulu wa Ansembe unalowedwera m’malo ndi udindo wa mkulu wa ansembe wa Chiyuda, onani nkhani yakuti, “Muziyamikira Mwayi Wanu Wolambira M’kachisi Wauzimu wa Yehova” mu Nsanja ya Olonda ya October 2023 tsamba 26, ndime 7-9.