Mawu a M'munsi
a Zikuoneka kuti Yobu anakhala ndi moyo pa nthawi imene mtumiki wokhulupirika Yosefe anamwalira (mu 1657 B.C.E.) kudzafika nthawi imene Mose anaikidwa kukhala mtsogoleri wa Aisiraeli. (cha m’ma 1514 B.C.E.) N’kutheka kuti nthawi imeneyi ndi imene Yehova ankakambirana ndi Satana zokhudza Yobu komanso ndi nthawi imene Yobuyo anakumana ndi mayesero.