Mawu a M'munsi
a MATANTHAUZO A MAWU ENA: M’zikhalidwe zambiri, pa tsiku la ukwati pamakhala mwambo umene anthu amene akukwatirana amalumbira pamaso pa Mulungu. Pambuyo pake pamakhala phwando la ukwati. M’madera amene sakhala ndi mwambo kapena phwando la ukwati, anthu amene akufuna kukwatirana angachite bwino kutsatira mfundo za m’Baibulo pa tsiku la ukwati wawo.