Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Poyamba dziko la Myanmar linkatchedwa Burma, potengera dzina la mtundu waukulu wa anthu a m’dzikoli, otchedwa Abamara (Abama). Dzinali analisintha mu 1989 n’kukhala Union of Myanmar (Mgwirizano wa Anthu a ku Myanmar). Anachita zimenezi pofuna kusonyeza kuti m’dzikoli mulinso mitundu ina yambiri ya anthu. M’buku lino tigwiritsa ntchito dzina lakuti Burma pofotokoza zinthu zomwe zinachitika chaka cha 1989 chisanafike ndipo tigwiritsa ntchito dzina lakuti Myanmar pofotokoza zinthu zomwe zinachitika chakachi chitadutsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena