Mawu a M'munsi
b Makaladi amene tikunena apa ndi anthu amene kholo lawo lina ndi Mmwenye pamene lina ndi lochokera ku Britain. Pa nthawi imene dzikoli linkalamuliridwa ndi dziko la Britain, amwenye ambiri anasamukira ku Burma ndipo ankatengedwa monga nzika za dzikolo.